Categories

معلومات المواد باللغة العربية

Islamic Creed

Number of Items: 2

  • chiCheŵa

    PDF

    Buku ili likukamba nsanamira zisanu ndi chimodzi za chikhulupiliro cha Msilamu. Layamba ndi kukamba mwachidule zomwe Msilamu amakhulupilira nthawi zonse, kenako lakamba zakomwe chikhulupilirochi chikuchokera (Qur’an ndi Sunnah). Nsanamira zimenezi ndimonga: Kukhulupilira Allah Yekha, kukhulupilira Angelo, kukhulupilira Mabuku a Allah, kukhulupilira Atumiki a Allah, kukhulupilira Tsiku Lachiweruzi ndinso kukhulupilira Chikhonzero cha Allah – komwe zabwino ndi zoipa zimachokera. Choncho buku ili ndi chiwongoko kwa okhulupilira komanso kwaomwe akufuna kukhulupilira.

  • chiCheŵa

    PDF

    Cholinga cha bukhuli ndi kuwaunikira anthu omwe amafuna kudziwa zoona zokhazokha, pa zauthenga weniweni womwe Yesu (mtendere ukhale pa iye) ankaphunzitsa. Bukhuli likukamba za machitidwe ena omwe analetsedwa kapena kuvomerezedwa m’Baibulo. Pali chikhulupiliro chakuti anthu akawerenga bukhuli adzipezera okha gulu lenileni la anthu lomwe limatsatira chiphunzitso cha Yesu (mtendere ukhale pa iye). Umboni wochokera m’Baibulo ugwiritsidwa ntchito pofuna kuwaunikira awerengi athu chipembedzo chenicheni cha Yesu (mtendere ukhale pa iye) lero lino. Anthuwa ayenera kudziwa otsatira enieni a chiphunzitso cha Baibulo.