Categories

معلومات المواد باللغة العربية

Islamic Jurisprudence

Number of Items: 2

  • chiCheŵa

    PDF

    Mu buku ili muli makomo awa: Kufunika kwa Swalaat, lamulo lake komanso zoyenereza kuti swalaat itheke. Machitidwe a wudhu kudzera m’zithunzi zolongosola bwino, kenako Sunnah za wudhu komanso zomwe zimaononga wudhu. Mu bukuli mulinso mapangidwe a Adhaan ndi Iqaamah, mapangidwe a swalaat kudzera m’zithunzi zolongosola bwino, komanso muli khomo la swalaat zisanu ndi swalaat zina za Sunnah. Komanso mukupezeka khomo la Twahara. Bukuli ndilofunikira kwambiri kwa omwe angolowa kumene Chisilamu, komanso Asilamu ena ongoyamba kumene kuphunzira.

  • chiCheŵa

    PDF

    Buku ili lasonkhanitsa kakhalidwe kwa amayi m’zipembedzo zitatu: Chiyuda, Chikristu ndi Chisilamu. Bukuli lalongosola mfundo zofunikira zochokera mu Chiyuda, komwe mzimayi sanangomutchula kuti ndi wochimwa, koma anatinso ndiyemwe anamuchimwitsa mwamuna. Koma Qur’an ili ndi kuwona kosiyana ndi mabuku ena onse, poti imamuona mzimai kuti ndi wofunikira kwambiri pa chitukuko cha munthu. Kumbali ya kuchimwa kapena kulungama, mzimai ali ndi kakhalidwe kofanana ndi mwamuna mchipembedzo; iye sichiyambi ya machismo onse. Bukuli lalongosola zokhudza Hijaab, ufulu wa kuphunzir kwa mkazi, ufulu wa kukhala ndi chuma chake pambuyo pa kukwatira, kulowa mmalo pambuyo pa kumwalira m’bale wake, mitala ndi nkhani zina. Awerengi a bukuli azindikira kusiyana komwe kulipo pakati pa Chisilamu ndi zipembedzo zina.