Categories

معلومات المواد باللغة العربية

How to Pray

Number of Items: 1

  • chiCheŵa

    PDF

    Mu buku ili muli makomo awa: Kufunika kwa Swalaat, lamulo lake komanso zoyenereza kuti swalaat itheke. Machitidwe a wudhu kudzera m’zithunzi zolongosola bwino, kenako Sunnah za wudhu komanso zomwe zimaononga wudhu. Mu bukuli mulinso mapangidwe a Adhaan ndi Iqaamah, mapangidwe a swalaat kudzera m’zithunzi zolongosola bwino, komanso muli khomo la swalaat zisanu ndi swalaat zina za Sunnah. Komanso mukupezeka khomo la Twahara. Bukuli ndilofunikira kwambiri kwa omwe angolowa kumene Chisilamu, komanso Asilamu ena ongoyamba kumene kuphunzira.