Categories

معلومات المواد باللغة العربية

Number of Items: 4

  • chiCheŵa

    PDF

    MALAMULO OFUNIKIRA KWA MSILAMU

  • chiCheŵa

    PDF

    Mu buku ili muli makomo awa: Kufunika kwa Swalaat, lamulo lake komanso zoyenereza kuti swalaat itheke. Machitidwe a wudhu kudzera m’zithunzi zolongosola bwino, kenako Sunnah za wudhu komanso zomwe zimaononga wudhu. Mu bukuli mulinso mapangidwe a Adhaan ndi Iqaamah, mapangidwe a swalaat kudzera m’zithunzi zolongosola bwino, komanso muli khomo la swalaat zisanu ndi swalaat zina za Sunnah. Komanso mukupezeka khomo la Twahara. Bukuli ndilofunikira kwambiri kwa omwe angolowa kumene Chisilamu, komanso Asilamu ena ongoyamba kumene kuphunzira.

  • chiCheŵa

    PDF

    Buku ili likukamba nsanamira zisanu ndi chimodzi za chikhulupiliro cha Msilamu. Layamba ndi kukamba mwachidule zomwe Msilamu amakhulupilira nthawi zonse, kenako lakamba zakomwe chikhulupilirochi chikuchokera (Qur’an ndi Sunnah). Nsanamira zimenezi ndimonga: Kukhulupilira Allah Yekha, kukhulupilira Angelo, kukhulupilira Mabuku a Allah, kukhulupilira Atumiki a Allah, kukhulupilira Tsiku Lachiweruzi ndinso kukhulupilira Chikhonzero cha Allah – komwe zabwino ndi zoipa zimachokera. Choncho buku ili ndi chiwongoko kwa okhulupilira komanso kwaomwe akufuna kukhulupilira.

  • chiCheŵa

    LINK

    QUR’AN YOLEMEKEZEKA yotanthauzidwa m’Chichewa ndi